Ezekiel 20:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
chifukwa sadamvere malamulo anga, adakana malangizo anga, adaipitsa masiku anga a Sabata, ndipo adapembedza mafano a makolo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
popeza sanachite maweruzo anga, koma ananyoza malemba anga, naipsa masabata anga, ndi maso ao anatsata mafano a atate ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
chifukwa sanamvere malamulo anga, anakana malangizo anga, nayipitsa masabata anga, ndi kupembedza mafano a makolo awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
popeza sanacita maweruzo anga, koma ananyoza malemba anga, naipsa masabata anga, ndi maso ao anatsata mafano a atate ao.