Ezekiel 21:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inenso ndidzaomba m'manja, ndi kuziziritsa mkwiyo wanga. Ine Chauta ndatero.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inenso ndidzaomba manja anga, ndipo ndidzakukwaniritsa ukali wanga; Ine Yehova ndanena.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inenso ndidzawomba mʼmanja mwanga, ndipo ndidzaziziritsa ukali wanga Ine Yehova ndayankhula.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inenso ndidzaomba manja anga, ndipo ndidzakukwaniritsa ukali wanga; Ine Yehova ndanena.