Ezekiel 21:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma kwa anthu a ku Yerusalemu zidzaoneka ngati zolosa zabodza, chifukwa cha malumbiro amene adaachita kwa mfumuyo. Koma adzaŵakumbutsa za machimo ao, kuti adzatengedwe ukapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzakhala ngati kuombeza konyenga pamaso pa iwo amene anawalumbirira malumbiro; koma akumbutsa mphulupulu kuti akodwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma kwa anthu a ku Yerusalemu zidzaoneka ngati zowombeza zabodza chifukwa cha malumbiro amene anachita kwa mfumuyo. Koma mfumuyo idzawakumbutsa za zolakwa zawo kuti atengedwe ku ukapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzakhala ngati kuombeza konyenga pamaso pa iwo amene anawalumbirira malumbiro; koma akumbutsa mphulupulu kuti akodwe.