Ezekiel 21:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimene ndikunena Ine Ambuye Chauta ndi izi: Vula nduŵirayo, chotsa chisoti chaufumucho. Zonse zasinthika! Otsika uŵakweze, okwera uŵatsitse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
atero Ambuye Yehova, Chotsa chilemba, vula korona, ufumu sudzakhalanso momwemo, kweza chopepuka, chepsa chokwezeka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ambuye Yehova akuti: Vula nduwira, chotsa chipewa chaufumu. Zinthu sizidzakhala monga zinalili: anthu wamba adzakwezedwa ndipo okwezedwa adzatsitsidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
atero Ambuye Yehova, Cotsa cilemba, bvula korona, ufumu sudzakhalanso momwemo, kweza copepuka, cepsa cokwezeka.