Ezekiel 21:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimene akuti akuziwona m'masomphenya nzabodza ndiponso maula ao ndi onama. Mudzakhala pamodzi ndi anthu oipa, amene tsiku lao lafika, ndiye kuti nthaŵi ya kulangidwa kwao komaliza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akuonera zopanda pake, akuombezera mabodza, lupanga likugoneka pa makosi a oipa olasidwa, amene lafika tsiku lao nthawi ya mphulupulu yotsiriza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zimene akuti akuona mʼmasomphenya zokhudza inu ndi zabodza. Mawula awo okhudza inu ndi abodzanso. Mudzakhala pamodzi ndi anthu oyipa amene tsiku lawo lafika, ndiye kuti nthawi ya kulangidwa kwawo komaliza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akuonera zopanda pace, akuombezera mabodza, lupanga likugoneka pa makosi a oipa olasidwa, amene lafika tsiku lao nthawi ya mphulupulu yotsiriza.