Ezekiel 21:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzakukwiyirani ndipo ukali wanga udzakuyakirani. Ndidzakuperekani m'manja mwa anthu ankhanza, amene amadziŵa kuwononga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndidzakutsanulira mkwiyo wanga, ndidzakuuzira ndi moto wa kuzaza kwanga, ndidzakuperekanso m'manja mwa anthu ankharwe odziwa kuononga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzakhuthula ukali wanga pa inu, ndipo mkwiyo wanga udzakuyakirani. Ndidzakuperekani mʼmanja mwa anthu ankhanza; anthu odziwa bwino kuwononga zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndidzakutsanulira mkwiyo wanga, ndidzakuuzira ndi moto wa kuzaza kwanga, ndidzakuperekanso m'manja mwa anthu ankharwe odziwa kuononga.