Ezekiel 21:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithu ndidzasolola lupanga langa m'chimake kuti ndidzaphe anthu ako oipa ndi abwino omwe, ndiye kuti anthu onse kuyambira kumwera mpaka kumpoto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Popeza ndidzakulikhira olungama ndi oipa, chifukwa chake lupanga langa lidzasololokera anthu onse, kuyambira kumwera kufikira kumpoto;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero ndidzapha aliyense kuchokera kummawa mpaka kumpoto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Popeza ndidzakulikhira olungama ndi oipa, cifukwa cace lupanga langa lidzasololokera anthu onse, kuyambira kumwera kufikira kumpoto;