Ezekiel 21:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero anthu onse adzadziŵa kuti Ine Chauta ndasolola lupanga langa, ndipo sindidzalilonganso m'chimake.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi anthu onse adzadziwa kuti Ine Yehova ndasolola lupanga langa m'chimake, silidzabwereranso.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo anthu onse adzadziwa kuti Ine Yehova ndi amene ndasolola lupanga langa mʼchimake; sindidzalilowetsanso mʼchimakemo.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi anthu onse adzadziwa kuti Ine Yehova ndasolola lupangalanga m'cimace, silidzabwereranso.