Ezekiel 24:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono uike pa makala mphika wopanda kanthuwo, kuti chitsulo chake chipse, kuchita kuti psuu. Zonyansa zake zonse zisungunuke, dzimbiri lichoke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo uukhazike pa makala ake opanda kanthu m'menemo, kuti utenthe, nuyake mkuwa wake; ndi kuti chodetsa chake chisungunuke m'mwemo, kuti dzimbiri lake lithe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono muyike pa makala mʼphika wopanda kanthuwo mpaka utenthe kuchita kuti psuu kuti zonyansa zake zisungunuke ndi kuti dzimbiri lake lichoke.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo uukhazike pa makara ace opanda kanthu m'menemo, kuti utenthe, nuyake mkuwa wace; ndi kuti codetsa cace cisungunuke m'mwemo, kuti dzimbiri lace lithe.