Ezekiel 27:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a ku Betetogarima ankapereka akavalo antchito, akavalo ankhondo ndi abulu mosinthana ndi katundu wako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwo a nyumba ya Togarima anagula malonda ako ndi akavalo, ndi akavalo a nkhondo, ndi nyuru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Anthu a ku Beti Togarima ankapereka akavalo antchito, akavalo ankhondo ndi abulu mosinthanitsa ndi katundu wako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwo a nyumba ya Togarima anagula malonda ako ndi akavalo, ndi akavalo a nkhondo, ndi nyuru.