Ezekiel 27:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a ku Dedani ankachita nawe malonda, anthunso a m'mbali mwa nyanja ankakupatsa minyanga ya njovu ndi phingo mosinthana ndi katundu wako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anthu a ku Dedani anakutsatsa malonda, zisumbu zambiri zinazolowerana nawe malonda ako, anabwera nazo minyanga ndi phingo kugulana nawe malonda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Anthu a ku Dedani ankachita nawe malonda, ndipo anthu ambiri a mʼmbali mwa nyanja anali ogula malonda ako. Ankakupatsa minyanga ya njovu ndi phingo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anthu a ku Dedani anakutsatsa malonda, zisumbu zambiri zinazolowerana nawe malonda ako, anabwera nazo minyanga ndi phingo kugulana nawe malonda.