Ezekiel 27:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malire ako ali m'kati mwenimweni mwa nyanja. Amisiri amene adakumanga, adakumanga ngati chombo chochititsa kaso zedi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'mphepete mwako muli m'kati mwa nyanja, iwo anakumanga iwe anakonza kukongola kwako kukhale kwangwiro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Malire ako anali mʼkati mwenimweni mwa nyanja; amisiri ako anakukongoletsa kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'mphepete mwako muli m'kati mwa nyanja, iwo anakumanga iwe anakonza kukongola kwako kukhale kwangwiro.