Ezekiel 27:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adakupanga ndi matabwa a mitengo ya paini ya ku phiri la Seniri. Adatenga mkungudza ku Lebanoni kuti adzapangire mlongoti wako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anacheka matabwa ako onse amlombwa wa ku Seniri, anatenga mikungudza ya ku Lebanoni kukupangira milongoti.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anakupanga ndi matabwa a payini ochokera ku Seniri; anatenga mikungudza ya ku Lebanoni kupangira mlongoti wako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anaceka matabwa ako onse amlombwa wa ku Seniri, anatenga mikungudza ya ku Lebano kukupangira milongoti.