Ezekiel 28:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidakuikira mngelo woopsa kuti azikulonda. Unkakhala pa phiri langa lopatulika, ndipo unkayenda pakati pa miyala yamoto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Unali kerubi wodzozedwa wakuphimba, ndipo ndinakuika unali pa phiri lopatulika la Mulungu, anayendayenda pakati pa miyala yamoto.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinayika kerubi kuti azikulondera. Unkakhala pa phiri langa lopatulika, ndipo unkayendayenda pakati pa miyala ya moto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Unali kerubi wodzozedwa wakuphimba, ndipo ndinakuika unali pa phiri lopatulika la Mulungu, anayendayenda pakati pa miyala yamoto.