Ezekiel 29:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Palibe phazi la munthu kapena la nyama limene lidzapondapo. Kudzakhala kopanda anthu pa zaka makumi anai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Silidzapitamo phazi la munthu, kapena phazi la nyama losapitamo, losakhalamo anthu zaka makumi anai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Palibe phazi la munthu kapena la nyama limene lidzapondepo. Kudzakhala kopanda anthu kwa zaka makumi anayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Silidzapitamo phazi la munthu, kapena phazi la nyama losapitamo, losakhalamo anthu zaka makumi anai.