Ezekiel 3:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Mulungu adandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, idya chimene ndikukupatsachi. Idya mpukutuwu ndipo pita ukalankhule ndi Aisraele.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ananena nane, Wobadwa ndi munthu iwe, Idya chimene wachipeza; idya mpukutu uwu, numuke ndi kunena ndi nyumba ya Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Mulungu anandiwuza kuti, “Mwana wa munthu, idya chimene ndikukupatsachi. Idya kenaka upite ukayankhule ndi Aisraeli.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ananena nane, Wobadwa ndi munthu iwe, Idya cimene wacipeza; idya mpukutu uwu, numuke ndi kunena ndi nyumba ya Israyeli.