Ezekiel 3:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsopano upite kwa Aisraele anzako amene ali ku ukapolo, ukalankhule nawo. Kaya akamvera kaya akakana, uzikaŵauza kuti, ‘Zimene akunena Ambuye Chauta nzakutizakuti,’ ”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Numuke, nufike kwa andende kwa ana a anthu a mtundu wako, nunene nao ndi kuwauza, Atero Yehova Mulungu, ngakhale akamva kapena akaleka kumva.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsopano upite kwa Aisraeli anzako amene ali ku ukapolo ndipo ukayankhule nawo. ‘Kaya akamvera kaya sakamvera,’ koma uzikawawuza kuti, Ambuye Wamphamvuzonse akuti zakutizakuti.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Numuke, nufike kwa andende kwa ana a anthu a mtundu wako, nunene nao ndi kuwauza, Atero Yehova Mulungu, ngakhale akamva kapena akaleka kumva.