Ezekiel 3:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Masiku asanu ndi aŵiriwo atatha, Chauta adandipatsira uthenga. Adati,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali atatha masiku asanu ndi awiri, mau a Yehova anandidzera, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atatha masiku asanu ndi awiriwo, Yehova anandiwuza kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali atatha masiku asanu ndi awiri, mau a Yehova anandidzera, ndi kuti,