Ezekiel 30:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anyamata a ku Oni ndi a ku Pibeseti adzaphedwa pa nkhondo, ndipo akazi adzatengedwa ukapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anyamata a Oni ndi Pibeseti adzagwa ndi lupanga, ndi midziyi idzalowa undende.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anyamata a ku Oni ndi ku Pibeseti adzaphedwa ndi lupanga ndipo okhala mʼmizinda yake adzatengedwa ukapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anyamata a Avene ndi Pibezeti adzagwa ndi lupanga, ndi midziyi idzalowa undende.