Ezekiel 30:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Etiopiya, Puti, Ludi, Arabiya yense, Libiya ndiponso anthu a m'dziko logwirizana naye, adzaphedwa nao limodzi pa nkhondoyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kusi, ndi Puti, ndi Ludi, ndi osokonezeka onse, ndi Libiya, ndi anthu a dziko lopangana nao, adzagwa pamodzi nao ndi lupanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kusi, Puti, Ludi ndi Arabiya yense, Libiya ndiponso anthu a mʼdziko logwirizana naye adzaphedwa ndi lupanga pamodzi ndi Igupto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kusi, ndi Puti, ndi Ludi, ndi osokonezeka onse, ndi Kubi, ndi anthu a dziko lopangana nao, adzagwa pamodzi nao ndi lupanga.