Ezekiel 31:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndidaupereka m'manja mwa mfumu yolamulira anthu a mitundu ina, kuti mfumuyo iwulange potsata zolakwa zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndidzaupereka m'dzanja la wamphamvu wa amitundu; iye adzachita naotu, Ine ndautaya mwa choipa chake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndinawupereka mʼdzanja la mfumu ya mitundu ya anthu kuti awulange molingana ndi kuyipa kwake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndidzaupereka m'dzanja la wamphamvu wa amitundu; iye adzacita naotu, Ine ndautaya mwa coipa cace.