Ezekiel 31:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Iwe mwana wa munthu, unene mau aŵa kwa Farao mfumu ya ku Ejipito pamodzi ndi gulu lake la nkhondo: “ ‘Kodi pa ukulu wanu nkukuyerekezani ndi yani?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wobadwa ndi munthu iwe, nena kwa Farao mfumu ya Aejipito ndi aunyinji ake, Ufanana ndi yani m'ukulu wako?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Iwe mwana wa munthu, unene kwa Farao mfumu ya Igupto ndi gulu lake lankhondo. Awawuze kuti, “ ‘Kodi mu ukulu wanu ndani angafanane ndi inu?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wobadwa ndi munthu iwe, nena kwa Farao mfumu ya Aigupto ndi aunyinji ace, Ufanana ndi yani m'ukulu wako?