Ezekiel 31:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Unali mtengo wokongola kwambiri wa nthambi zitalizitali, chifukwa choti mizu yake inkazama ndi kulandira madzi ambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'mwemo unakoma m'ukulu wake, m'kutalika kwa nthawi zake, popeza muzu wake unakhala kumadzi ambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Unali wokongola kwambiri, wa nthambi zake zotambalala, chifukwa mizu yake inazama pansi kumene kunali madzi ochuluka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'mwemo unakoma m'ukulu wace, m'kutalika kwa nthawi zace, popeza muzu wace unakhala ku madzi ambiri.