Ezekiel 31:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndi Ineyo Mulungu amene ndidaukongoletsa, pochulukitsa nthambi zake, kotero kuti mitengo yonse ya mu Edeni, munda wa Mulungu inkachita nawo nsanje.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinaupanga wokoma ndi nthawi zake zochuluka; ndi mitengo yonse ya m'Edeni inali m'munda wa Mulungu inachita nao nsanje.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinawupanga wokongola wa nthambi zochuluka. Mitengo yonse ya mu Edeni, mʼmunda wa Mulungu inawuchitira nsanje.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinaupanga wokoma ndi nthawi zace zocuruka; ndi mitengo yonse ya m'Edene inali m'munda wa Mulungu inacita nao nsanje.