Ezekiel 33:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Komabe anthu a mtundu wako amati, ‘Zimene Chauta amachitazi nzopanda chilungamo.’ Iyai, koma makhalidwe ao ndiwo amene ali osalungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ana a anthu a mtundu wako akuti, Njira ya Ambuye siiyenera; koma iwowa njira yao siiyenera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Komabe anthu a mtundu wako akunena kuti, ‘Zimene Ambuye amachita ndi zopanda chilungamo.’ Ayi, koma makhalidwe awo ndiwo ali osalungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ana a anthu a mtundu wako akuti, Njira ya Ambuye siiyenera; koma iwowa njira yao siiyenera.