Ezekiel 33:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikadzalanga anthu chifukwa cha zonyansa zimene adachita, ndi kusandutsa dzikolo kuti likhale tsala ndiponso chipululu, pamenepo adzadziŵa kuti Ine ndine Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, posanduliza Ine dziko likhale lachipululu ndi lodabwitsa, chifukwa cha zonyansa zao zonse anazichita.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndikadzasandutsa dzikolo chipululu chifukwa cha zonyansa zimene ankachita, pamenepo ndiye adzadziwa kuti ndine Yehova.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, posanduliza Ine dziko likhale lacipululu ndi lodabwitsa, cifukwa ca zonyansa zao zonse anazicita.