Ezekiel 34:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zofooka mumaziwomba ndi kuzikankhira kumbali, ndipo mumazigunda ndi nyanga zanu nkuzimwazira kutali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Popeza mukankha ndi nthiti ndi phewa, nimugunda zodwala zonse ndi nyanga zanu, mpaka mwazibalalitsa kubwalo,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza zofowoka mumaziwomba ndi kuzikankhira kumbali, ndipo mumazigunda ndi nyanga zanu nʼkuzimwazira kutali,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Popeza mukankha ndi nthiti ndi phewa, nimugunda zodwala zonse ndi nyanga zanu, mpaka mwazibalalitsa kubwalo,