Ezekiel 37:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndiyang'ane, ndidaona kuti pali mitsempha, kenaka mnofu ukuwonekanso, potsiriza nkubwera khungu pamwamba pake, koma munalibe mpweya mwa iwo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinapenya, taonani, panali mitsempha pa iwo, panadzaponso mnofu, ndi khungu linawakuta pamwamba pake; koma munalibe mpweya mwa iwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinayangʼana, ndipo mitsempha ndi mnofu zinabwera pa mafupawo ndipo khungu linaphimba pamwamba pake, koma munalibe mpweya mwa iwo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinapenya, taonani, panali mitsempha pa iwo, panadzaponso mnofu, ndi khungu linawakuta pamwamba pace; koma munalibe mpweya mwa iwo.