Ezekiel 39:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ku phwando lansembe limene ndikukukonzeranilo, mudzadya zonona mpaka kukhuta, mudzamwa magazi mpaka kuledzera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mudzadya zonona mpaka mudzakhuta, ndi kumwa mwazi mpaka mudzaledzera za nsembe yanga ndakupherani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ku phwando lansembe limene ndikukonzera inulo, mudzadya zonona mpaka kukhuta ndi kumwa magazi mpaka kuledzera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mudzadya zonona mpaka mudzakhuta, ndi kumwa mwazi mpaka mudzaledzera za nsembe yanga ndakupherani.