Ezekiel 39:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo akadzakhazikika mwamtendere m'dziko lao, popanda wina woŵavuta, pamenepo adzaiŵala zamanyazi zao zimene zidaŵagwera chifukwa chosandikhulupirira Ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo adzasenza manyazi ao, ndi zolakwa zao zonse, zimene anandilakwira nazo, pokhala mosatekeseka iwo m'dziko lao, opanda wina wakuwaopsa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthuwo akadzakhala mwamtendere mʼdziko lawo popanda wina wowaopseza, pamenepo adzayiwala zamanyazi zawo zimene zinawachitikira chifukwa chosandikhulupirira Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo adzasenza manyazi ao, ndi zolakwa zao zonse, zimene anandilakwira nazo, pokhala mosatekeseka iwo m'dziko lao, opanda wina wakuwaopsa;