Ezekiel 39:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzagwetsa moto pa dziko la Magogi ndi pa onse amene amakhala mwamtendere m'mbali mwa nyanja. Motero adzadziŵa kuti Ine ndine Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndidzatumizira moto Magogi, ndi iwo okhala mosatekeseka m'zisumbu; motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzatumiza moto pa Magogi ndi pa onse amene amakhala mwamtendere mʼmbali mwa nyanja. Choncho adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndidzatumizira moto Magogi, ndi iwo okhala mosatekeseka m'zisumbu; motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.