Ezekiel 4:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndachitatu kukuikira masiku, okwanira 390, kulinganiza ndi zaka za machimo ao. Umu ndimo m'mene udzasenzere machimo a Aisraele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Ine ndakuikira zaka za mphulupulu yao ngati masiku, ndiwo masiku mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai, kuti usenze mphulupulu ya nyumba ya Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndakuyikira masiku okwana 390 malingana ndi zaka za machimo awo. Umu ndi mmene udzasenzere machimo a Aisraeli.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Ine ndakuikira zaka za mphulupulu yao ngati masiku, ndiwo masiku mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai, kuti usenze mphulupulu ya nyumba ya Israyeli.