Ezekiel 4:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithudi, ndidzakumanga ndi zingwe, kotero kuti sudzatha kutembenukira uku ndi uku, mpaka kuzingidwa kwa Yerusalemu kutatha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo taona ndidzakumanga ndi zingwe zolimba kuti usakunkhulire, mpaka watsiriza masiku a kuzingidwa kwako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndidzakumanga ndi zingwe kotero kuti sudzatha kutembenukira uku ndi uku mpaka utatsiriza masiku akuzingidwa ako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo taona ndidzakumanga ndi zingwe zolimba kuti usakunkhulire, mpaka watsiriza masiku a kuzingidwa kwako.