Ezekiel 40:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake adayesa khonde lam'kati, linali la mamita khumi. Ndipo pozungulira khondelo panali bwalo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anamanganso nsanamira za mikono makumi asanu ndi limodzi; ndi bwalo la pakati pa chipata lidafikira kunsanamira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anayezanso khonde lamʼkati ndipo linali la mamita makumi atatu. Ndipo mozungulira khondelo munali bwalo. Muyesowu sukuphatikiza khonde loyangʼanana ndi bwalo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anamanganso nsaaamira za mikono makumi asanu ndi limodzi; ndi bwalo la pakati pa cipata lidafikira kunsanamira.