Ezekiel 42:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo kunsi kwa zipinda zakumwera, kunali khomo lake mbali ya kuvuma kumene ankaloŵerako. Kunalinso khoma logaŵa zipinda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi monga mwa makomo a zipinda za kumwera panali khomo polekeza njira, ndiyo njira yokhudzana ndi linga la kum'mawa polowamo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndi makomo a zipinda zakummwera. Kunali khomo mʼmbali ya kummawa kumene ankalowerako. Kunalinso khoma logawa zipinda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi monga mwa makomo a zipinda za kumwela panali khomo polekeza njira, ndiyo njira yokhudzana ndi linga la kum'mawa polowamo.