Ezekiel 42:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero adayesa mbali zonse zinai. Panali khoma lozungulira bwalo lonselo, m'litali mwake linali la mamita 250, muufupi mwakenso mamita 250. Khomalo linali lolekanitsa zinthu zoyera ndi zinthu wamba.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Analiyesa mbali zake zinai, linali nalo linga pozungulira pake, utali wake mikono mazana asanu, chitando chake mikono mazana asanu, kusiyanitsa pakati pa zopatulika ndi zinthu wamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero anayeza mbali zonse zinayi. Panali khoma lozungulira bwalolo mulitali mwake munali mamita 250 ndipo mulifupi mwake munalinso mamita 250. Khomalo linali lolekanitsa zinthu zoyera ndi zinthu wamba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Analiyesa mbali zace zinai, linali nalo linga pozungulira pace, utali wace mazana asanu, citando cace mazana asanu, kusiyanitsa pakati pa zopatulika ndi zawamba.