Ezekiel 42:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kumaso kwa zipindazo kunali njira yam'kati, muufupi mwake mamita asanu, m'litali mwake mamita makumi asanu. Makomo ake adaaloza kumpoto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi kukhomo kwa zipinda anakonza poyendapo, kupingasa kwake mikono khumi m'kati mwake, njira ya mikono zana limodzi, ndi makomo ao analoza kumpoto.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumaso kwa zipindazo kunali njira yamʼkati, mulifupi mwake munali mamita asanu, mulitali mwake munali mamita makumi asanu. Makomo ake analoza chakumpoto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi kukhomo kwa zipinda anakonza poyendapo, kupingasa kwace mikono khumi m'kati mwace, njira ya mikono zana limodzi, ndi makomo ao analoza kumpoto.