Ezekiel 42:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zonse zinali zosanjikana patatu, ndipo zinalibe nsanamira monga za mabwalo. Motero zipinda zam'mwamba zinali zochepera kuyerekeza ndi zapakati ndi zapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti zinasanjikizana pawiri, ndipo zinalibe nsanamira ngati nsanamira za kumabwalo; chifukwa chake zam'mwambazo zinachepa koposa zakunsi ndi pakati kuyambira pansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza zipinda zinali zosanjikizana katatu ndipo zinalibe nsanamira monga za mabwalo, motero zipinda zamʼmwamba zinali zochepa kuyerekeza ndi zipinda zapansi ndi zipinda zapakati.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti zinasanjikizana pawiri, ndipo zinalibe nsanamira ngati nsanamira za kumabwalo; cifukwa cace zam'mwambazo zinacepa koposa zakunsi ndi zapakati kuyambira pansi.