Ezekiel 43:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kumeneko ndidaona ulemerero wa Mulungu wa Israele ukuchokera kuvuma. Liwu lake linali ngati mkokomo wa madzi, ndipo dziko lapansi lidaŵala ndi ulemerero wakewo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo taonani, ulemerero wa Mulungu wa Israele unadzera njira ya kum'mawa, ndi mau ake ananga mkokomo wa madzi ambiri, ndi dziko linanyezimira ndi ulemerero wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo ndinaona ulemerero wa Mulungu wa Israeli ukubwera kuchokera kummawa. Liwu lake linali ngati mkokomo wamadzi, ndipo dziko linawala ndi ulemerero wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo taonani, ulemerero wa Mulungu wa Israyeli unadzera njira ya kum'mawa, ndi mau ace ananga mkokomo wa madzi ambiri, ndi dziko linanyezimira ndi ulemerero wace.