Ezekiel 44:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati aipitsidwa kenaka nkuyeretsedwa, adikire masiku asanu ndi aŵiri, kuti akhale woyeretsedwa kotheratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo atayeretsedwa amwerengere masiku asanu ndi awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atatha kuyeretsedwa adikirebe masiku asanu ndi awiri kuti ayere ndithu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo atayeretsedwa amwerengere masiku asanu ndi awiri.