Ezekiel 46:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsiku lililonse, nthaŵi yam'maŵa, azipereka kwa Chauta mwanawankhosa wa chaka chimodzi wopanda chilema.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Uziperekanso kwa Yehova mwanawankhosa wa chaka chimodzi akhale nsembe yopsereza wopanda chilema, tsiku ndi tsiku, m'mawa ndi m'mawa, uzimpereka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsiku lililonse nthawi ya mmawa azipereka kwa Yehova mwana wankhosa wa chaka chimodzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Uziperekanso kwa Yehova mwana wa nkhosa wa caka cimodzi akhale nsembe yopsereza wopanda cirema, tsiku ndi tsiku, m'mawa ndi m'mawa, uzimpereka.