Ezekiel 46:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuzungulira mabwalo anai ang'onoang'onowo panali mpanda wamiyala, ndiponso malo osonkhapo moto, omangidwa m'munsi mwa mpandawo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali maguwa pozungulira pake m'menemo, pozungulira pake pa mabwalo anai; ndipo anamanga maguwawo ndi mafuwa pansi pake pozungulirapo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuzungulira mabwalo anayi angʼonoangʼono aja panali mpanda wamiyala, ndi malo asonkhapo moto omangidwa mʼmunsi mwa mpandawo mozungulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali maguwa pozungulira pace m'menemo, pozungulira pace pa mabwalo anai; ndipo anamanga maguwawo ndi mafuwa pansi pace pozungulirapo.