Ezekiel 5:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono mwa inu makolo adzadya ana ao ndipo ana adzadya makolo ao. Ndidzakulanganidi, ndipo onse otsala pakati pa inu, ndidzaŵamwazira ku mphepo zonse zinai.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake atate adzadya ana pakati pako, ndi ana adzadya atate ao; ndipo ndidzachita maweruzo mwa iwe, ndi akutsala onse ndidzawabalalitsa kumphepo zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono pakati panu makolo adzadya ana awo, ndipo ana adzadya makolo awo. Ndidzakulanga ndipo otsala onse ndidzawabalalitsa ku mphepo zonse zinayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace atate adzadya ana pakati pako, ndi ana adzadya atate ao; ndipo ndidzacita maweruzo mwa iwe, ndi akutsala onse ndidzawabalalitsa ku mphepo zonse.