Ezekiel 6:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Komabe ena mwa inu ndidzaŵasiya amoyo. Adzapulumuka ku nkhondo, ndipo ndidzaŵamwazira ku maiko ena, pakati pa anthu a mitundu ina.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ndidzasiyapo otsala, popeza mudzakhala nao ena akupulumuka lupanga mwa amitundu pobalalitsidwa inu m'maiko maiko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Komabe ndidzasiya ena pangʼono opulumuka ku nkhondo. Iwowa ndidzawamwazira ku mayiko ena pakati pa anthu a mitundu ina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ndidzasiyapo otsala, popeza mudzakhala nao ena akupulumuka lupanga mwa amitundu pobalalitsidwa inu m'maiko maiko.