Ezekiel 7:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Onanitu tsiku latsoka! Onanitu chikubwera! Chilango chanu chafika. Kunyada kwanu kwakakata, kudzitama kwanu kwaonekera poyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taona, tsikuli, taona, lafika; tsoka lako latuluka, ndodo yaphuka mphundu za maluwa, kudzitama kwaphuka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taona, tsikulo! Taona, lafika! Chiwonongeko chako chabwera. Ndodo yaphuka mphundu za maluwa. Kudzitama kwaphuka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taona, tsikuli, taona, lafika; tsoka lako laturuka, ndodo yaphuka mphundu za maluwa, kudzitama kwaphuka.