Ezekiel 7:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nthaŵi yafika, tsiku layandikira. Wogula asakondwe, ndipo wogulitsa asamve chisoni, pakuti ukali wanga waŵagwera onse chimodzimodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yafika nthawi, layandikira tsikulo, wogula asakondwere, ndi wogulitsa asamve chisoni; pakuti mkwiyo ukhalira unyinji wao wonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi yafika! Tsiku layandikira! Munthu wogula asakondwere ndipo wogulitsa asamve chisoni, popeza ukali wanga uli pa gulu lonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yafika nthawi, layandikira tsikulo, wogula asakondwere, ndi wogulitsa asamve cisoni; pakuti mkwiyo ukhalira unyinji wao wense.