Ezekiel 7:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndidzaŵalekerera anthuwo, kuti adzaipitse malo anga okondedwa. Adzaloŵamo ngati mbala nkuipitsamo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo nkhope yanga idzawayang'anira kumbali, ndipo iwo adzadetsa pobisika panga, nadzalowamo achifwamba, nadzamudetsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndidzawalekerera anthuwo ndipo adzayipitsa malo anga apamtima. Adzalowamo ngati mbala ndi kuyipitsamo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo nkhope yanga idzawayang'anira kumbali, ndipo iwo adzadetsa pobisika panga, nadzalowamo acifwamba, nadzamudetsa.