Ezekiel 7:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Konzani maunyolo, popeza kuti anthu opha anzao achuluka m'dziko, mzinda wadzaza ndi ndeu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sula unyolo, popeza dziko ladzala ndi milandu yamwazi, ndi mudzi wadzala ndi chiwawa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Konzani maunyolo, chifukwa dziko ladzaza ndi anthu opha anzawo ndipo mzinda wadzaza ndi chiwawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sula unyolo, popeza dziko ladzala ndi mirandu yamwazi, ndi mudzi wadzala ndi ciwawa.