Ezekiel 7:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chimalizo chafika, chimalizo chija chafika! Chakugwera, ndithu chabwera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kutha kwafika, kwafika kutha. Kwakugalamukira, taona kwafika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chimaliziro chafika! Chimaliziro chafika! Chiwonongeko chakugwera. Taona chafika!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kutha kwafika, kwafika kutha, kwakugalamukira, taona kwafika.