Ezekiel 7:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Posachedwapa ndidzakukwiyirani, ndipo ukali wanga udzathera pa inu. Ndidzagamula mlandu wanu potsata makhalidwe anu, ndipo ndidzakulangani chifukwa cha zonyansa zanu zochuluka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Katsala kamphindi, ndipo ndidzakutsanulira ukali wanga, ndi kukukwaniritsira mkwiyo wanga, ndi kukuweruza monga mwa njira zako, ndipo ndidzakubwezera zonyansa zako zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndili pafupi kukukwiyirani, ndipo ukali wanga udzathera pa iwe; Ine ndidzakuweruza molingana ndi machitidwe ako ndiponso ndidzakulanga chifukwa cha miyambo yako yonyansa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Katsala kamphindi, ndipo ndidzakutsanulira ukali wanga, ndi kukukwaniritsira mkwiyo wanga, ndi kukuweruza monga mwa njira zako, ndipo ndidzakubwezera zonyansa zako zonse.